2 Mafumu 21:9 - Buku Lopatulika9 Koma sanamvere, nawalakwitsa Manase, nawachititsa choipa, kuposa amitundu amene Yehova adawaononga pamaso pa ana a Israele. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Koma sanamvere, nawalakwitsa Manase, nawachititsa choipa, kuposa amitundu amene Yehova adawaononga pamaso pa ana a Israele. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Koma anthuwo sadamve zimenezo, ndipo Manase adaŵasokeretsa ndi kuŵachimwitsa kwambiri kupambana anthu a mitundu ina amene Chauta adaŵaononga pofika Aisraele. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Koma anthu sanamvere. Manase anawasocheretsa, kotero kuti anachita zoyipa zambiri kupambana anthu a mitundu ina amene Yehova anawawononga pamene Aisraeli ankafika. Onani mutuwo |