2 Mafumu 21:5 - Buku Lopatulika5 Nalimangira khamu lonse la kuthambo maguwa a nsembe m'mabwalo awiri a nyumba ya Yehova. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Nalimangira khamu lonse la kuthambo maguwa a nsembe m'mabwalo awiri a nyumba ya Yehova. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Manase yemweyo adamangira zinthu zakuthambo maguwa m'mabwalo aŵiri a Nyumba ya Chauta. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Mʼmabwalo onse awiri a Nyumba ya Yehova, Manase anamangamo maguwa opembedzerapo zinthu zamlengalenga. Onani mutuwo |
Ndipo mfumu inalamulira Hilikiya mkulu wa ansembe, ndi ansembe a gawo lachiwiri, ndi olindira pakhomo, atulutse mu Kachisi wa Yehova zipangizo adazipangira Baala, ndi chifanizo adazipangira Baala, ndi chifanizo chija, ndi khamu lonse la kuthambo; nazitentha kunja kwa Yerusalemu ku thengo la ku Kidroni, natenga phulusa lake kunka nalo ku Betele.