2 Mafumu 21:4 - Buku Lopatulika4 Namanga iye maguwa a nsembe m'nyumba ya Yehova imene Yehova adainenera kuti, Mu Yerusalemu ndidzaika dzina langa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Namanga iye maguwa a nsembe m'nyumba ya Yehova imene Yehova adainenera kuti, M'Yerusalemu ndidzaika dzina langa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Adamangira mafanowo maguwa m'Nyumba ya Chauta imene Chautayo adaanena kuti, “Ku Yerusalemu ndiye kumene azikandipembedzerako.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Anamanga maguwa ansembewa mʼNyumba ya Yehova, mʼmene Yehova ananena kuti, “Mu Yerusalemu ndidzayikamo Dzina langa.” Onani mutuwo |