2 Mafumu 21:23 - Buku Lopatulika23 Ndipo anyamata ake a Amoni anamchitira chiwembu, napha mfumuyo m'nyumba yakeyake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201423 Ndipo anyamata ake a Amoni anamchitira chiwembu, napha mfumuyo m'nyumba yakeyake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa23 Tsono anyamata ake adamchita chiwembu, namupha m'nyumba mwake momwe. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero23 Nduna za Amoni zinamuchita chiwembu ndipo zinamupha mʼnyumba yake. Onani mutuwo |