2 Mafumu 21:22 - Buku Lopatulika22 nasiya Yehova Mulungu wa makolo ake, sanayende m'njira ya Yehova. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201422 nasiya Yehova Mulungu wa makolo ake, sanayende m'njira ya Yehova. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa22 Adakana Chauta, Mulungu wa makolo ake, ndipo sadamvere malamulo ake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero22 Iyeyo anasiya Yehova Mulungu wa makolo ake ndipo sanayende mʼnjira ya Yehova. Onani mutuwo |