2 Mafumu 21:2 - Buku Lopatulika2 Ndipo anachita choipa pamaso pa Yehova, monga mwa zonyansa za amitundu amene Yehova anawaingitsa pamaso pa ana a Israele. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Ndipo anachita choipa pamaso pa Yehova, monga mwa zonyansa za amitundu amene Yehova anawaingitsa pamaso pa ana a Israele. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Iyeyo adachita zoipa pamaso pa Chauta, potsata ntchito zonyansa za anthu a mitundu ina amene Chauta adaŵapirikitsa pofika Aisraele. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Iye anachita zoyipa pamaso pa Yehova, potsatira mchitidwe wonyansa wa mitundu imene Yehova anayipirikitsa pofika Aisraeli. Onani mutuwo |