2 Mafumu 21:1 - Buku Lopatulika1 Manase anali wa zaka khumi ndi ziwiri polowa iye ufumu wake, nakhala mfumu zaka makumi asanu ndi zisanu mu Yerusalemu; ndi dzina la make ndiye Hepeziba. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Manase anali wa zaka khumi ndi ziwiri polowa iye ufumu wake, nakhala mfumu zaka makumi asanu ndi zisanu m'Yerusalemu; ndi dzina la make ndiye Hepeziba. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Manase anali wa zaka khumi ndi ziŵiri pamene adaloŵa ufumu, ndipo adalamulira zaka 55 ku Yerusalemu. Mai wake anali Hepeziba. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Manase anakhala mfumu ali ndi zaka khumi ndi ziwiri ndipo analamulira mu Yerusalemu zaka 55. Amayi ake anali Hefiziba. Onani mutuwo |