2 Mafumu 20:9 - Buku Lopatulika9 Nati Yesaya, Chizindikiro ndichi akupatsa Yehova, kuti Yehova adzachichita chonena Iye; kodi mthunzi umuke m'tsogolo makwerero khumi, kapena ubwerere m'mbuyo makwerero khumi? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Nati Yesaya, Chizindikiro ndichi akupatsa Yehova, kuti Yehova adzachichita chonena Iye; kodi mthunzi umuke m'tsogolo makwerero khumi, kapena ubwerere m'mbuyo makwerero khumi? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Yesaya adayankha kuti, “Chizindikiro chimene Chauta wakupatsa chakuti adzachitadi zimene adalonjeza nachi: Kodi chithunzithunzi chipite patsogolo kapena chibwerere pambuyo makwerero khumi?” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Yesaya anayankha kuti, “Chizindikiro cha Yehova chosonyeza kuti Iye adzachita chimene walonjeza ndi ichi: Kodi chithunzithunzi chipite patsogolo kapena chibwerere pambuyo makwerero khumi?” Onani mutuwo |