2 Mafumu 20:7 - Buku Lopatulika7 Nati Yesaya, Tenga nchinchi yankhuyu. Naitenga, naiika pafundo, nachira iye. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Nati Yesaya, Tenga nchinchi yankhuyu. Naitenga, naiika pafundo, nachira iye. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Pambuyo pake Yesaya adauza antchito a mfumu kuti, “Konzani phala lankhuyu. Kenaka mutengeko phalalo nkulimata pa chithupsa chake, kuti mfumu ichire.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Pamenepo Yesaya anati, “Konzani phala lankhuyu.” Iwo anakonza phalalo nalipaka pa chithupsacho ndipo Hezekiya anachira. Onani mutuwo |