2 Mafumu 20:4 - Buku Lopatulika4 Ndipo kunali, asanatulukire Yesaya m'kati mwa mudzi, anamdzera mau a Yehova, ndi kuti, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Ndipo kunali, asanatulukire Yesaya m'kati mwa mudzi, anamdzera mau a Yehova, ndi kuti, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Tsono Yesaya asanatuluke m'bwalo lapakati, Chauta adamuuza kuti, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Yesaya asanatuluke mʼbwalo lapakati, Yehova anayankhula kuti, Onani mutuwo |