2 Mafumu 20:10 - Buku Lopatulika10 Nati Hezekiya, Kutsikira mthunzi makwerero khumi nkopepuka, kutero ai; koma mthunzi ubwerere makwerero khumi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Nati Hezekiya, Kutsikira mthunzi makwerero khumi nkopepuka, kutero ai; koma mthunzi ubwerere makwerero khumi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Hezekiyayo adayankha kuti, “Nchapafupi kuti chithunzithunzi chipite patsogolo makwerero khumi, koma kuti chithunzithunzicho chibwerere m'mbuyo makwerero khumi, apo ndiponi.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Hezekiya anati, “Nʼchapafupi kuti chithunzithunzi chipite patsogolo makwerero khumi, kulekana nʼkuti chithunzithunzicho chibwerere mʼmbuyo makwerero khumi.” Onani mutuwo |