2 Mafumu 2:7 - Buku Lopatulika7 Ndipo anthu makumi asanu a ana a aneneri anapita, naima patali pandunji pao, iwo awiri naima ku Yordani. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Ndipo anthu makumi asanu a ana a aneneri anapita, naima patali pandunji pao, iwo awiri naima ku Yordani. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Anthu makumi asanu a m'gulu la aneneri aja adapita nawo ndipo adakaimirira chapatali potero, pamene Eliya ndi Elisa adaakaima pa gombe la mtsinje wa Yordani. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Anthu makumi asanu mwa ana a aneneri anawatsatira nayima chapatali moyangʼanana nawo ndipo Eliya ndi Elisa anayima mʼmphepete mwa Yorodani. Onani mutuwo |