Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




2 Mafumu 2:22 - Buku Lopatulika

22 Chotero madzi anachiritsidwa mpaka lero lino, monga mwa mau a Elisa ananenawo.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

22 Chotero madzi anachiritsidwa mpaka lero lino, monga mwa mau a Elisa ananenawo.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

22 Motero madziwo ngabwinobe kwambiri mpaka lero lino, potsata mau amene Elisa adaalankhula.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

22 Kotero madziwo ndi abwino mpaka lero, molingana ndi mawu amene Elisa anayankhula.

Onani mutuwo Koperani




2 Mafumu 2:22
2 Mawu Ofanana  

Ndipo anatuluka kunka ku magwero a madzi, nathiramo mchere, nati, Atero Yehova, Ndachiritsa madzi awa, sikudzafumirakonso imfa, kapena kusabalitsa.


Ndipo anachokako kukwera ku Betele, ndipo iye ali chikwerere m'njiramo, munatuluka anyamata aang'ono m'mzindamo, namseka, nati kwa iye, Takwera wadazi, takwera wadazi!


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa