Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




2 Mafumu 2:20 - Buku Lopatulika

20 Pamenepo anati, Nditengereni chotengera chatsopano, muikemo mchere. Ndipo anabwera nacho kwa iye.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

20 Pamenepo anati, Nditengereni chotengera chatsopano, muikemo mchere. Ndipo anabwera nacho kwa iye.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

20 Apo Elisa adati, “Patseni mbale yatsopano, ndipo muikemo mchere.” Anthuwo adabweradi ndi mchere m'mbale.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

20 Iye anati, “Patseni mbale yatsopano ndipo muyikemo mchere.” Ndipo anabweretsa mbaleyo kwa iye.

Onani mutuwo Koperani




2 Mafumu 2:20
5 Mawu Ofanana  

Ndipo amuna amumzinda anati kwa Elisa, Taonani, mumzinda muno m'mwabwino, monga umo aonera mbuye wanga; koma madzi ndi oipa, ndi nthaka siibalitsa.


Ndipo anatuluka kunka ku magwero a madzi, nathiramo mchere, nati, Atero Yehova, Ndachiritsa madzi awa, sikudzafumirakonso imfa, kapena kusabalitsa.


Koma pali matope ake ndi zithaphwi zake sipadzakonzeka, paperekedwa pakhale pamchere.


Chifukwa chake, pali moyo wanga, ati Yehova wa makamu, Mulungu wa Israele, Zedi Mowabu adzakhala ngati Sodomu, ndi ana a Amoni ngati Gomora, pochuluka khwisa ndi maenje a mchere, ndi bwinja losatha; otsala a anthu anga adzalanda zao, ndi otsala a mtundu wa anthu anga adzawalandira akhale cholowa chao.


Ndipo Abimeleki analimbana ndi mzinda tsiku lija lonse; nalanda mzinda nawapha anthu anali m'mwemo; napasula mzinda; nawazapo mchere.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa