2 Mafumu 2:19 - Buku Lopatulika19 Ndipo amuna amumzinda anati kwa Elisa, Taonani, mumzinda muno m'mwabwino, monga umo aonera mbuye wanga; koma madzi ndi oipa, ndi nthaka siibalitsa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201419 Ndipo amuna akumudzi anati kwa Elisa, Taonani, pamudzi pano mpabwino, monga umo aonera mbuye wanga; koma madzi ndi oipa, ndi nthaka siibalitsa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa19 Tsiku lina anthu amumzinda adauza Elisa kuti, “Onani, mzinda wathuwu ngwabwino kwambiri, zonse zili bwino monga mukuwoneramu, koma madzi okha ngoipa, ndipo nthaka yake njosabereka.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero19 Anthu a mu mzindamo anati kwa Elisa, “Mbuye wathu, taonani mzinda uno uli pamalo pabwino, monga mukuoneramu, koma madzi ake ndi oyipa, nthaka yakenso ndi yosabereka.” Onani mutuwo |