2 Mafumu 2:18 - Buku Lopatulika18 Nabwerera kwa iye ali chikhalire ku Yeriko, ndipo anati kwa iwo, Kodi sindinanene nanu, Musamuka? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 Nabwerera kwa iye ali chikhalire ku Yeriko, ndipo anati kwa iwo, Kodi sindinanena nanu, Musamuka? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 Tsono adabwerera kwa Elisayo pamene iyeyo ankadikira ku Yeriko, ndipo iye adaŵauza kuti, “Kodi suja ndidaanena kuti musapite?” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 Atabwerera kwa Elisa (chifukwa anali akanali ku Yeriko), iye anawawuza kuti, “Kodi sindinakuwuzeni kuti musapite?” Onani mutuwo |