2 Mafumu 2:13 - Buku Lopatulika13 Pamenepo anatola chofunda chake cha Eliya chidamtayikiracho, nabwerera, naima m'mphepete mwa Yordani. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Pamenepo anatola chofunda chake cha Eliya chidamtayikiracho, nabwerera, naima m'mphepete mwa Yordani. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Kenaka adatenga mwinjiro wa Eliya umene udaagwa, nabwerera nkukaima pa gombe la Yordani. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Iye anatola chovala cha Eliya chomwe chinagwa nabwerera ndi kukayima mʼmphepete mwa Yorodani. Onani mutuwo |