Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




2 Mafumu 19:5 - Buku Lopatulika

5 Ndipo anyamata a mfumu Hezekiya anafika kwa Yesaya.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

5 Ndipo anyamata a mfumu Hezekiya anafika kwa Yesaya.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

5 Pamene Yesaya adamva mau a mfumu Hezekiyawo,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

5 Akuluakulu a Mfumu Hezekiya atafika kwa Yesaya,

Onani mutuwo Koperani




2 Mafumu 19:5
4 Mawu Ofanana  

Kapena Yehova Mulungu wanu adzamva mau onse a kazembeyo, amene anamtuma mfumu ya Asiriya mbuye wake, kuti atonze Mulungu wamoyo, nadzamlanga chifukwa cha mau adawamva Yehova Mulungu wanu; chifukwa chake uwakwezere otsalawo pemphero.


Nanena nao Yesaya, Muzitero kwa mbuye wanu, Atero Yehova, Musamaopa mau mudawamva, amene anyamata a mfumu ya Asiriya anandichitira nao mwano.


Ndipo Yesaya anati kwa iwo, Mukati kwa mbuyanu, Atero Yehova, musaope mau amene wawamva iwe, amene atumiki a mfumu ya Asiriya andilalatira Ine.


Imvani, Israele; Yehova Mulungu wathu, Yehova ndiye mmodzi;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa