2 Mafumu 19:11 - Buku Lopatulika11 Taona, udamva icho mafumu a Asiriya anachitira maiko onse, ndi kuwaononga konse; ndipo uti upulumuke ndiwe kodi? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Taona, udamva icho mafumu a Asiriya anachitira maiko onse, ndi kuwaononga konse; ndipo uti upulumuke ndiwe kodi? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Wakhala ulikumva zimene mafumu a ku Asiriya adaŵachita maiko onse, kuti adaŵaononga kotheratu. Tsono iweyo ndiye nkupulumuka? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Ndithu iwe unamva chimene mafumu a Asiriya anachita ku mayiko ena onse, kuti anawawononga kotheratu. Ndipo kodi iwe nʼkupulumuka? Onani mutuwo |