2 Mafumu 19:1 - Buku Lopatulika1 Ndipo kunali, atamva mfumu Hezekiya, anang'amba zovala zake, nafundira chiguduli, nalowa m'nyumba ya Yehova. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Ndipo kunali, atamva mfumu Hezekiya, anang'amba zovala zake, nafundira chiguduli, nalowa m'nyumba ya Yehova. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Hezekiya atangomva zimenezi, adang'amba zovala zake mwachisoni, ndipo adavala chiguduli, nakaloŵa m'Nyumba ya Chauta. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Mfumu Hezekiya atamva zimenezi, anangʼamba zovala zake navala chiguduli ndipo analowa mʼNyumba ya Yehova. Onani mutuwo |