2 Mafumu 18:8 - Buku Lopatulika8 Anakantha Afilisti mpaka Gaza ndi malire ake, kuyambira nsanja ya olonda mpaka mzinda walinga. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Anakantha Afilisti mpaka Gaza ndi malire ake, kuyambira nsanja ya olonda mpaka mudzi walinga. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Adakantha Afilisti mpaka ku Gaza ndi ku dera lake lonse. Adaononga mudzi uliwonse ndi mzinda uliwonse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Iye anakantha Afilisti kuyambira ku nsanja ya alonda mpaka ku mzinda wotetezedwa. Anakafika mpaka ku Gaza ndi ku malire ake. Onani mutuwo |