2 Mafumu 18:7 - Buku Lopatulika7 Ndipo Yehova anali naye, nachita iye mwanzeru kulikonse anamukako, napandukira mfumu ya Asiriya osamtumikira. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Ndipo Yehova anali naye, nachita iye mwanzeru kulikonse anamukako, napandukira mfumu ya Asiriya osamtumikira. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Nchifukwa chake Chauta anali naye. Kulikonse kumene ankapita, zinthu zinkamuyendera bwino. Hezekiyayo adapandukira mfumu ya ku Asiriya, mwakuti sankaitumikiranso ai. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Ndipo Yehova anali naye ndipo kulikonse kumene anapita zinthu zinkamuyendera bwino. Iye anagalukira mfumu ya ku Asiriya ndipo sanayitumikirenso. Onani mutuwo |