Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




2 Mafumu 18:2 - Buku Lopatulika

2 Ndiye wa zaka makumi awiri ndi zisanu polowa ufumu wake, nakhala mfumu zaka makumi awiri mphambu zisanu ndi zinai mu Yerusalemu; ndi dzina la make ndiye Abi mwana wa Zekariya.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

2 Ndiye wa zaka makumi awiri ndi zisanu polowa ufumu wake, nakhala mfumu zaka makumi awiri mphambu zisanu ndi zinai m'Yerusalemu; ndi dzina la make ndiye Abi mwana wa Zekariya.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

2 Anali wa zaka 25 pamene adaloŵa ufumu, ndipo adalamulira zaka 29 ku Yerusalemu. Mai wake anali Abi, mwana wa Zekariya.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

2 Anakhala mfumu ali ndi zaka 25 ndipo analamulira mu Yerusalemu zaka 29. Amayi ake anali Abi, mwana wa Zekariya.

Onani mutuwo Koperani




2 Mafumu 18:2
2 Mawu Ofanana  

Ukanene kwa Hezekiya, Atero Yehova, Mulungu wa Davide, kholo lako, Ndamva kupemphera kwako, ndaona misozi yako; taona, ndidzaonjezera pa masiku ako zaka khumi ndi zisanu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa