2 Mafumu 17:9 - Buku Lopatulika9 Ndipo ana a Israele anachita m'tseri zinthu zosayenera pa Yehova Mulungu wao, nadzimangira misanje m'mizinda mwao monse kunsanja ya olonda ndi kumzinda walinga komwe. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Ndipo ana a Israele anachita m'tseri zinthu zosayenera pa Yehova Mulungu wao, nadzimangira misanje m'midzi mwao monse kunsanja ya olonda ndi kumudzi walinga komwe. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Ndipo Aisraele ankachita zinthu zoipa mobisika namachimwira Chauta Mulungu wao. Adadzimangira akachisi opembedzerako mafano ku midzi yao yonse ndi ku mizinda yomwe. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Ndipo Aisraeli ankachita zoyipa mwamseri kutsutsana ndi Yehova Mulungu wawo. Kuchokera ku nsanja ya alonda mpaka ku mzinda wotetezedwa, mʼmizinda yawo yonse anamangamo malo opembedzeramo mafano. Onani mutuwo |