2 Mafumu 17:5 - Buku Lopatulika5 Pamenepo mfumu ya Asiriya anakwera m'dziko monse, nakwera ku Samariya, naumangira misasa zaka zitatu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Pamenepo mfumu ya Asiriya anakwera m'dziko monse, nakwera ku Samariya, naumangira misasa zaka zitatu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Nthaŵi yomweyo Salimanezere, mfumu ya ku Asiriya, adathira nkhondo dziko la Israele nakafika ku Samariya, nkukauzinga mzindawo ndi zithando zankhondo zaka zitatu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Mfumu ya ku Asiriya inapita kukathira nkhondo dziko lonse la Israeli ndipo inapita mpaka ku Samariya ndipo inazinga mzindawo kwa zaka zitatu. Onani mutuwo |