2 Mafumu 17:40 - Buku Lopatulika40 Koma sanamvere, nachita monga mwa mwambo wao woyamba. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201440 Koma sanamvere, nachita monga mwa mwambo wao woyamba. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa40 Komabe iwowo sankamva zimenezi, koma ankachitabe zimene adakhala akuchita kuyambira kale. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero40 Komabe iwo sanamvere ndipo anapitiriza kuchita zomwe ankachita kale. Onani mutuwo |