2 Mafumu 17:12 - Buku Lopatulika12 natumikira mafano amene Yehova anawanena nao, Musachita ichi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 natumikira mafano amene Yehova anawanena nao, Musachita ichi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Tsono adapembedza mafano kuchimwira Chauta amene anali ataŵauza kuti, “Musadzachite zimenezi.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Ndipo iwowo ankapembedza mafano ngakhale Yehova ananena kuti, “Musadzachite zimenezi.” Onani mutuwo |