Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




2 Mafumu 17:12 - Buku Lopatulika

12 natumikira mafano amene Yehova anawanena nao, Musachita ichi.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

12 natumikira mafano amene Yehova anawanena nao, Musachita ichi.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

12 Tsono adapembedza mafano kuchimwira Chauta amene anali ataŵauza kuti, “Musadzachite zimenezi.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

12 Ndipo iwowo ankapembedza mafano ngakhale Yehova ananena kuti, “Musadzachite zimenezi.”

Onani mutuwo Koperani




2 Mafumu 17:12
13 Mawu Ofanana  

Ndipo anachita moipitsitsa kutsata mafano, monga mwa zonse amazichita Aamori, amene Yehova adawapirikitsa pamaso pa ana a Israele.


nafukizapo zonunkhira pa misanje yonse, monga umo amachitira amitundu amene Yehova adawachotsa pamaso pao, nachita zoipa kuutsa mkwiyo wa Yehova;


Koma sanamvere, nachita monga mwa mwambo wao woyamba.


Ine ndine Yehova Mulungu wako, amene ndinatulutsa iwe ku dziko la Ejipito, kunyumba ya ukapolo.


pakuti musalambira mulungu wina; popeza Yehova dzina lake ndiye Wansanje, ali Mulungu wansanje;


Nditafika nao m'dzikolo ndinawakwezera dzanja langa kuwapatsa ilo, anapenya chitunda chilichonse chachitali, ndi mtengo uliwonse wagudugudu, naphera pomwepo nsembe zao, naperekapo nsembe zao zondiputa, aponso anachita fungo lao lokoma, nathiraponso nsembe zao zothira.


Musamadzipangira mafano, kapena kudziutsira mafano osema, kapena choimiritsa, kapena kuika mwala wozokota m'dziko mwanu kuugwadira umenewo; popeza Ine ndine Yehova Mulungu wanu.


Musamatero ndi Yehova Mulungu wanu.


osalowa pakati pa amitundu awa otsala mwa inu; kapena kutchula dzina la milungu yao; osalumbiritsa nalo, kapena kuitumikira, kapena kuigwadira;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa