2 Mafumu 17:10 - Buku Lopatulika10 Nadziimikira zoimiritsa ndi zifanizo pa chitunda chilichonse chachitali, ndi patsinde pa mtengo uliwonse wogudira; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Nadziimikira zoimiritsa ndi zifanizo pa chitunda chilichonse chachitali, ndi patsinde pa mtengo uliwonse wogudira; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Adadzimangira zipilala zoimiritsa ndiponso mafano pa phiri lililonse lalitali ndi patsinde pa mitengo yogudira. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Anayimika miyala ya chipembedzo ndi mitengo ya mafano a Asera pa phiri lililonse lalitali ndi pansi pa mtengo uliwonse wa masamba ambiri. Onani mutuwo |