2 Mafumu 16:9 - Buku Lopatulika9 Nimmvera mfumu ya Asiriya, nikwera kunka ku Damasiko mfumu ya Asiriya, niulanda, nipita nao anthu ake andende ku Kiri, nimupha Rezini. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Nimmvera mfumu ya Asiriya, nikwera kunka ku Damasiko mfumu ya Asiriya, niulanda, nipita nao anthu ake andende ku Kiri, nimupha Rezini. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Tsono mfumu ya ku Asiriya idamvera Ahazi ndipo idakathira nkhondo Damasiko nilanda mzindawo ndi kupha Rezini. Anthu ake idaŵatenga ukapolo kupita nawo ku Kiri. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Mfumu ya ku Asiriya inamvera pokathira nkhondo mzinda wa Damasiko ndi kuwulanda. Anthu a mu mzindamo anawatumiza ku Kiri ndipo anapha Rezini. Onani mutuwo |