Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




2 Mafumu 16:6 - Buku Lopatulika

6 Nthawi yomweyo Rezini mfumu ya Aramu anabwezera Elati kwa Aramu, napirikitsa Ayuda ku Elati; nadza Aaramu ku Elati, nakhala komwemo kufikira lero lino.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

6 Nthawi yomweyo Rezini mfumu ya Aramu anabwezera Elati kwa Aramu, napirikitsa Ayuda ku Elati; nadza Aaramu ku Elati, nakhala komwemo kufikira lero lino.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

6 Nthaŵi imeneyo Rezini mfumu ya ku Edomu adapirikitsa Ayuda ku Elati, nalanda mzindawo, kuubwezera kwa Aedomu, ndipo iwo adakhala kumeneko mpaka lero lino.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

6 Nthawi imeneyo Rezini mfumu ya Aramu anatenganso Elati ndi kumubwezera kwa Aaramu, nathamangitsa anthu a ku Yuda mu Elatimo. Aedomu anapita kukakhala ku Elati ndipo akukhalako mpaka lero lino.

Onani mutuwo Koperani




2 Mafumu 16:6
4 Mawu Ofanana  

Ndipo mfumu Solomoni anamanga zombo zambiri ku Eziyoni-Gebere uli pafupi ndi Eloti, m'mphepete mwa Nyanja Yofiira, ku dziko la Edomu.


Anamanga Elati, naubweza kwa Yuda, mfumuyo itagona ndi makolo ake.


Iye anamanga Eloti, naubweza kwa Yuda, mfumuyo itagona ndi makolo ake.


Potero tinapitirira abale athu, ana a Esau okhala mu Seiri, njira ya chidikha, ku Elati ndi ku Eziyoni-Gebere. Pamenepo tinatembenuka ndi kudzera njira ya chipululu cha Mowabu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa