2 Mafumu 16:5 - Buku Lopatulika5 Pamenepo Rezini mfumu ya Aramu, ndi Peka mwana wa Remaliya mfumu ya Israele, anakwera kunka ku Yerusalemu kukachita nkhondo, nammangira Ahazi misasa; koma sanakhoze kumgonjetsa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Pamenepo Rezini mfumu ya Aramu, ndi Peka mwana wa Remaliya mfumu ya Israele, anakwera kunka ku Yerusalemu kukachita nkhondo, nammangira Ahazi misasa; koma sanakhoze kumgonjetsa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Tsono Rezini mfumu ya ku Siriya ndi Peka mwana wa Remaliya mfumu ya ku Israele adabwera kudzathira nkhondo Yerusalemu namzinga Ahazi ndi zithando zankhondo, koma sadathe kumgonjetsa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Ndipo Rezini mfumu ya Aramu ndi Peka mwana wa Remaliya mfumu ya Israeli anapita kukachita naye nkhondo ku Yerusalemu ndipo anazinga Ahazi, koma sanathe kumugonjetsa. Onani mutuwo |