2 Mafumu 16:3 - Buku Lopatulika3 popeza anayenda m'njira ya mafumu a Israele, napititsanso mwana wake pamoto, monga mwa zonyansa za amitundu amene Yehova anawaingitsa pamaso pa ana a Israele. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 popeza anayenda m'njira ya mafumu a Israele, napititsanso mwana wake pamoto, monga mwa zonyansa za amitundu amene Yehova anawaingitsa pamaso pa ana a Israele. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Koma adatsata zitsanzo zoipa za mafumu a ku Israele. Adapereka mwana wake wamwamuna ngati nsembe yopsereza potsatira miyambo yonyansa ya anthu a mitundu ina imene Chauta adaaipirikitsa m'dzikomo pamene ankafika Aisraele. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Iye anayenda mʼnjira ya mafumu a Israeli mpaka kupereka mwana wake wamwamuna pa moto ngati nsembe yopsereza, potsatira zonyansa za anthu a mitundu imene Yehova anayipirikitsa mʼdzikomo Aisraeli asanafike. Onani mutuwo |