2 Mafumu 16:16 - Buku Lopatulika16 Nachita Uriya wansembe monga mwa zonse adalamulira mfumu Ahazi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 Nachita Uriya wansembe monga mwa zonse adalamulira mfumu Ahazi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Tsono wansembe Uriya adachita zonsezo, monga momwe mfumu Ahazi adaalamulira. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 Ndipo wansembe Uriya anachita monga analamulira Mfumu Ahazi. Onani mutuwo |
Ndipo mfumu Ahazi analamulira Uriya wansembe, kuti, Paguwa la nsembe lalikulu uzifukiza nsembe yopsereza yam'mawa, ndi nsembe yaufa yamadzulo, ndi nsembe yopsereza ya mfumu, ndi nsembe yake yaufa, pamodzi ndi nsembe yopsereza ya anthu onse a m'dziko, ndi nsembe yao yaufa, ndi nsembe zao zothira; uziwaza pa ilo mwazi wonse wa nsembe yopsereza, ndi mwazi wonse wa nsembe yophera; koma guwa la nsembe lamkuwa ndi langa, lofunsira nalo.