2 Mafumu 16:12 - Buku Lopatulika12 Atafika mfumu kuchokera ku Damasiko, anapenya mfumu guwa la nsembelo, nayandikiza mfumu ku guwa la nsembelo, napereka nsembe pomwepo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Atafika mfumu kuchokera ku Damasiko, anapenya mfumu guwa la nsembelo, nayandikiza mfumu ku guwa la nsembelo, napereka nsembe pomwepo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Mfumu itabwera kuchokera ku Damasiko, nipenya guwa lija, idasendera pafupi ndi guwalo ndi kukwera kuguwako. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Mfumu itabwera kuchokera ku Damasiko kuja ndi kuona guwalo, inasendera pafupi ndi kupereka nsembe paguwapo. Onani mutuwo |