2 Mafumu 16:1 - Buku Lopatulika1 Chaka chakhumi mphambu zisanu ndi ziwiri cha Peka mwana wa Remaliya Ahazi mwana wa Yotamu mfumu ya Yuda analowa ufumu wake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Chaka chakhumi mphambu zisanu ndi ziwiri cha Peka mwana wa Remaliya Ahazi mwana wa Yotamu mfumu ya Yuda analowa ufumu wake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Chaka cha 17 cha ufumu wa Peka mwana wa Remaliya, Ahazi mwana wa Yotamu mfumu ya ku Yuda, adaloŵa ufumu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Mʼchaka cha 17 cha Peka mwana wa Remaliya, Ahazi mwana wa Yotamu mfumu ya Yuda anayamba kulamulira. Onani mutuwo |