2 Mafumu 15:8 - Buku Lopatulika8 Chaka cha makumi atatu mphambu zisanu ndi zitatu cha Azariya mfumu ya Yuda, Zekariya mwana wa Yerobowamu anakhala mfumu ya Israele mu Samariya miyezi isanu ndi umodzi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Chaka cha makumi atatu mphambu zisanu ndi zitatu cha Azariya mfumu ya Yuda, Zekariya mwana wa Yerobowamu anakhala mfumu ya Israele m'Samariya miyezi isanu ndi umodzi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Chaka cha 38 cha ufumu wa Azariya mfumu ya ku Yuda, Zekariya mwana wa Yerobowamu, adaloŵa ufumu wa Aisraele ku Samariya kwa miyezi isanu ndi umodzi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Mʼchaka cha 38 cha Azariya mfumu ya Yuda, Zekariya mwana wa Yeroboamu anakhala mfumu ya Israeli ku Samariya ndipo analamulira miyezi isanu ndi umodzi. Onani mutuwo |