Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




2 Mafumu 15:6 - Buku Lopatulika

6 Machitidwe ena tsono a Azariya, ndi zonse anazichita, sizinalembedwe kodi m'buku la machitidwe a mafumu a Yuda?

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

6 Machitidwe ena tsono a Azariya, ndi zonse anazichita, sizinalembedwa kodi m'buku la machitidwe a mafumu a Yuda?

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

6 Tsono ntchito zina za Azariya ndi zonse zimene adazichita, zidalembedwa m'buku la Mbiri ya Mafumu a ku Yuda.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

6 Ntchito zina za Azariya ndi zonse zimene anachita, kodi sizinalembedwe mʼbuku la mbiri ya mafumu a Yuda?

Onani mutuwo Koperani




2 Mafumu 15:6
6 Mawu Ofanana  

Tsono, machitidwe ake ena a Rehobowamu, ndi zonse anazichita, sizinalembedwe kodi m'buku la machitidwe a mafumu a Yuda?


Machitidwe ena tsono a Amaziya, sanalembedwe kodi m'buku la machitidwe a mafumu a Yuda?


Ndipo Yehova anadwaza mfumu, nakhala iye wakhate mpaka tsiku la imfa yake, nakhala m'nyumba ya padera. Ndipo Yotamu mwana wa mfumu anayang'anira banja la mfumu, naweruza anthu a m'dziko.


Nagona Azariya ndi makolo ake, namuika ndi makolo ake m'mzinda wa Davide; nakhala mfumu m'malo mwake Yotamu mwana wake.


Ndi machitidwe ena a Yoramu, ndi zonse anazichita, sizinalembedwe kodi m'buku la machitidwe a mafumu a Yuda.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa