2 Mafumu 15:4 - Buku Lopatulika4 Komatu sanaichotse misanje; anthu anapherabe nsembe, nafukiza pamisanje. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Komatu sanaichotse misanje; anthu anapherabe nsembe, nafukiza pamisanje. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Komabe akachisi opembedzerako mafano pa zitunda sadaŵaononge. Anthu ankaperekabe nsembe ndi kumafukiza lubani pa malo amenewo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Komabe malo opembedzerako mafano sanawachotse ndipo anthu anapitirizabe kupereka nsembe ndi kufukiza lubani kumeneko. Onani mutuwo |