Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




2 Mafumu 15:34 - Buku Lopatulika

34 Nachita iye zoongoka pamaso pa Yehova; anachita monga mwa zonse anazichita atate wake Uziya.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

34 Nachita iye zoongoka pamaso pa Yehova; anachita monga mwa zonse anazichita atate wake Uziya.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

34 Yotamu adachita zolungama pamaso pa Chauta ndipo kutsata zonse zimene ankachita Uziya bambo wake.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

34 Iye anachita zabwino pamaso pa Yehova monga anachitira Uziya abambo ake.

Onani mutuwo Koperani




2 Mafumu 15:34
3 Mawu Ofanana  

Ndipo anachita zoongoka pamaso pa Yehova, monga umo adachitira atate wake Uziya; pokhapo sanalowe mu Kachisi wa Yehova. Koma anthu anachitabe zovunda.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa