2 Mafumu 15:22 - Buku Lopatulika22 Nagona Menahemu ndi makolo ake; nakhala mfumu m'malo mwake Pekahiya mwana wake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201422 Nagona Menahemu ndi makolo ake; nakhala mfumu m'malo mwake Pekahiya mwana wake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa22 Ndipo Menahemu adamwalira, naikidwa m'manda momwe adaikidwa makolo akewo. Tsono Pekahiya mwana wake adaloŵa ufumu m'malo mwake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero22 Menahemu anamwalira ndipo anayikidwa mʼmanda pamodzi ndi makolo ake. Ndipo Pekahiya mwana wake analowa ufumu mʼmalo mwake. Onani mutuwo |