2 Mafumu 15:12 - Buku Lopatulika12 Awa ndi mau a Yehova anawanena ndi Yehu, ndi kuti, Ana ako kufikira mbadwo wachinai adzakhala pa mpando wachifumu wa Israele. Ndipo kunatero momwemo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Awa ndi mau a Yehova anawanena ndi Yehu, ndi kuti, Ana ako kufikira mbadwo wachinai adzakhala pa mpando wachifumu wa Israele. Ndipo kunatero momwemo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Izi ndi zimene Chauta adalonjeza Yehu, adati, “Ana ako aamuna adzalamulira Aisraele mpaka mbadwo wachinai.” Ndipo zidachitikadi momwemo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Awa ndiwo mawu a Yehova amene anayankhula kwa Yehu kuti, “Ana ako adzalamulira Israeli mpaka mʼbado wachinayi.” Onani mutuwo |