2 Mafumu 15:11 - Buku Lopatulika11 Machitidwe ena tsono a Zekariya, taonani, zalembedwa m'buku la machitidwe a mafumu a Israele. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Machitidwe ena tsono a Zekariya, taonani, zalembedwa m'buku la machitidwe a mafumu a Israele. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Tsono ntchito zonse zimene adachita Zekariya zidalembedwa m'buku la Mbiri ya Mafumu a Israele. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Ntchito zina za Zekariya, zinalembedwa mʼbuku la mbiri ya mafumu a Israeli. Onani mutuwo |