2 Mafumu 15:10 - Buku Lopatulika10 Ndipo Salumu mwana wa Yabesi anamchitira chiwembu, namkantha pamaso pa anthu, namupha; nakhala mfumu m'malo mwake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Ndipo Salumu mwana wa Yabesi anamchitira chiwembu, namkantha pamaso pa anthu, namupha; nakhala mfumu m'malo mwake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Tsono Salumu mwana wa Yabesi adamchita chiwembu Zekariya, ndipo adamphera ku Ibleamu. Choncho Salumuyo adaloŵa ufumu m'malo mwake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Salumu mwana wa Yabesi anachitira chiwembu Zekariya. Anamukantha anthu akuona, namupha, ndipo analowa ufumu mʼmalo mwake. Onani mutuwo |