Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




2 Mafumu 14:8 - Buku Lopatulika

8 Pamenepo Amaziya anatuma mithenga kwa Yehowasi mwana wa Yehowahazi mwana wa Yehu mfumu ya Israele, ndi kuti, Idzani tionane maso.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

8 Pamenepo Amaziya anatuma mithenga kwa Yehowasi mwana wa Yehowahazi mwana wa Yehu mfumu ya Israele, ndi kuti, Idzani tionane maso.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

8 Nthaŵi ina Amaziya adatuma amithenga kwa Yehowasi mwana wa Yehowahazi, mdzukulu wa Yehu, mfumu ya ku Israele, kukanena momputa kuti, “Ubwere kuno, tidzaonane maso ndi maso.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

8 Tsono Amaziya anatuma amithenga kwa Yehowasi mwana wa Yehowahazi, mwana wa Yehu mfumu ya Israeli ndi kumuopseza kuti, “Bwera tidzaonane maso ndi maso.”

Onani mutuwo Koperani




2 Mafumu 14:8
12 Mawu Ofanana  

Nati iye, Chinkana atulukira mumtendere, agwireni amoyo; chinkana atulukira m'nkhondo, agwireni, amoyo.


Machitidwe ena tsono a Yowasi, ndi zonse anazichita, ndi mphamvu yake yochita nkhondo nayo pa Amaziya mfumu ya Yuda, sizinalembedwe kodi m'buku la machitidwe a mafumu a Israele?


Koma Amaziya sanamvere. Motero anakwera Yehowasi mfumu ya Israele, ndipo iye ndi Amaziya mfumu ya Yuda anapenyana maso ku Betesemesi, ndiwo wa Yuda.


Ndipo kunali, atafika Amaziya atatha kuwapha Aedomu, ndi kubwera nayo milungu ya ana a Seiri, anaiika ikhale milungu yake, naigwadira, naifukizira.


Kudzikuza kupikisanitsa; koma omwe anauzidwa uphungu ali ndi nzeru.


Chiyambi cha ndeu chifanana ndi kutsegulira madzi; tsono kupikisana kusanayambe tasiya makani.


Milomo ya wopusa ifikitsa makangano; ndipo m'kamwa mwake muputa kukwapulidwa.


Uphungu utsimikiza zolingalira, ponya nkhondo utapanga upo.


Usatuluke mwansontho kukalimbana, ungalephere pa kutha kwake, atakuchititsa mnzako manyazi.


Mwenzi anthu awa akadakhala m'dzanja langa; ndikadamchotsadi Abimeleki. Ndipo anati kwa Abimeleki, Chulukitsa khamu lako, nutuluke.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa