2 Mafumu 14:7 - Buku Lopatulika7 Anapha Aedomu mu Chigwa cha Mchere zikwi khumi, nalanda Sela ndi nkhondo, nautcha dzina lake Yokotele mpaka lero lino. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Anapha Aedomu m'Chigwa cha Mchere zikwi khumi, nalanda Sela ndi nkhondo, nautcha dzina lake Yokotele mpaka lero lino. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Tsono Amaziya adaphanso Aedomu okwanira 10,000 ku chigwa cha Mchere, nalanda mzinda wa Sela, ndipo adautchula dzina lakuti Yokitele, ndipo dzina lake ndi lomwelo mpaka pano. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Iye ndiye amene anapha Aedomu 10,000 mʼchigwa cha Mchere nalanda mzinda wa Sela pa nkhondo ndipo anawutcha Yokiteeli, dzina lake ndi lomwelo mpaka lero lino. Onani mutuwo |