Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




2 Mafumu 14:4 - Buku Lopatulika

4 Koma misanje sanaichotse; anthu anapherabe nsembe, nafukiza pamisanje.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

4 Koma misanje sanaichotse; anthu anapherabe nsembe, nafukiza pamisanje.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

4 Koma akachisi opembedzerako mafano pa zitunda sadaŵaononge. Anthu adapitirirabe kupereka nsembe ndi kumafukiza lubani pa malo amenewo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

4 Komabe sanachotse malo opembedzerapo mafano. Anthu anapitiriza kupereka nsembe ndi kufukiza lubani kumeneko.

Onani mutuwo Koperani




2 Mafumu 14:4
6 Mawu Ofanana  

Koma misanje sanaichotse; anthu anapherabe nsembe, nafukiza kumisanje.


Ndipo Yowasi anati kwa ansembe, Landirani ndalama zonse za zinthu zopatulika azibwera nazo kunyumba ya Yehova, ndizo ndalama za otha msinkhu, ndalama za munthu aliyense monga adamuyesa, ndi ndalama zimene yense azikumbuka m'mtima mwake kuti abwere nazo kunyumba ya Yehova.


Ndipo anachita zoongoka pamaso pa Yehova, koma wosanga Davide kholo lake; nachita monga mwa zonse anazichita Yowasi atate wake.


Komatu sanaichotse misanje; anthu anapherabe nsembe, nafukiza pamisanje. Iye anamanga chipata cha kumtunda cha nyumba ya Yehova.


Komatu sanaichotse misanje; anthu anapherabe nsembe, nafukiza pamisanje.


Ndipo anaphera nsembe, nafukiza zonunkhira kumisanje, ndi kuzitunda, ndi patsinde pa mtengo uliwonse wogudira.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa