2 Mafumu 14:3 - Buku Lopatulika3 Ndipo anachita zoongoka pamaso pa Yehova, koma wosanga Davide kholo lake; nachita monga mwa zonse anazichita Yowasi atate wake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Ndipo anachita zoongoka pamaso pa Yehova, koma wosanga Davide kholo lake; nachita monga mwa zonse anazichita Yowasi atate wake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Tsono Amaziya adachita zolungama pamaso pa Chauta, komabe osati nthaŵi zonse monga Davide kholo lake. Ankachita zonse monga m'mene ankachitira Yowasi bambo wake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Iye anachita zolungama pamaso pa Yehova, koma osafanana ndi zomwe anachita Davide kholo lake. Iye anatsatira zochita zonse za Yowasi abambo ake. Onani mutuwo |