2 Mafumu 14:18 - Buku Lopatulika18 Machitidwe ena tsono a Amaziya, sanalembedwe kodi m'buku la machitidwe a mafumu a Yuda? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 Machitidwe ena tsono a Amaziya, sanalembedwa kodi m'buku la machitidwe a mafumu a Yuda? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 Tsono ntchito zina zonse zimene adachita Amaziya zidalembedwa m'buku la Mbiri ya Mafumu a ku Yuda. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 Ntchito zina za Amaziya, kodi sizinalembedwe mʼbuku la mbiri ya mafumu a Yuda? Onani mutuwo |