2 Mafumu 13:15 - Buku Lopatulika15 Nanena naye Elisa, Tenga uta ndi mivi; nadzitengera uta ndi mivi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201415 Nanena naye Elisa, Tenga uta ndi mivi; nadzitengera uta ndi mivi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa15 Pamenepo Elisa adauza Yehowasi kuti, “Tengani uta ndi mivi yake.” Adatenga utawo ndi miviyo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero15 Elisa anamuwuza kuti, “Tenga uta ndi mivi.” Ndipo anaterodi. Onani mutuwo |