2 Mafumu 13:13 - Buku Lopatulika13 Ndipo Yowasi anagona ndi makolo ake, ndi Yerobowamu anakhala pa mpando wachifumu wake; namuika Yowasi mu Samariya pamodzi ndi mafumu a Israele. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Ndipo Yowasi anagona ndi makolo ake, ndi Yerobowamu anakhala pa mpando wachifumu wake; namuika Yowasi m'Samariya pamodzi ndi mafumu a Israele. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Motero Yehowasi adamwalira, naikidwa ku Samariya pamodzi ndi mafumu a ku Israele. Tsono Yerobowamu mwana wake adaloŵa ufumu m'malo mwake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Yowasi anayikidwa mʼmanda pamodzi ndi makolo ake ndipo Yeroboamu mwana wake analowa ufumu mʼmalo mwake. Yowasi anayikidwa mʼmanda mu Samariya pamodzi ndi mafumu a Israeli. Onani mutuwo |